HIS EXCELLENCY DR LAZARUS MCCARTHY CHAKWERA.
Francis Yolam -
4
Chakwera anthu amamuziwa ngati munthu odekha osakonda zolakhulalakhul<br>a,munthu owopa Mulungu,munthu okwanilisa lonjezo lake komanso munthu okonda anthu osayang'ana mbali. Chinaso chodabwsa ndi chakuti a MEC atanena kuti a Chakwera apambana a Chakwera asayambe kunyadila anayamba Kaye kupemphera kuthokoza Mulungu ndipo post yawo yawo pa page pa FB Iwo anati "Zikomo ambuye wanga,Yesu" zomwe zikupasa anthu chiyembekezo kuti President ameneyi ndiwoopa Mulungu ndipo akwanisa zofuna zawo. Chakwera akhala President wa number 6 wadziko la Malawi ndipo alamulira kwa zaka zisanu 2020-2025.. A Chakwera amakondaso mpira ndipo amasapota Mighty Be forward Wanderers komanso Arsenal.